Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Magaleta a Farao ndi magulu ake ankhondo wawaponyera m’nyanja.+

      Asilikali a Farao osankhidwa mwapadera amizidwa mu Nyanja Yofiira.+

  • Yobu 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndi mphamvu zake wavundula nyanja,+

      Ndipo ndi kuzindikira kwake wathyolathyola+ wachiwawa.*+

  • Salimo 87:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ine ndidzatchula Rahabi*+ ndi Babulo+ monga ena mwa amene akundidziwa.

      Ponena za Filisitiya,+ Turo ndi Kusi ine ndidzati:

      “Amenewa anabadwira m’Ziyoni.”+

  • Salimo 89:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwaphwanya Rahabi*+ ndi kumuchititsa kukhala ngati munthu amene waphedwa.+

      Mwabalalitsa adani anu ndi dzanja lanu lamphamvu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena