Ekisodo 14:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Kenako Yehova anauza Mose kuti: “Tambasula dzanja lako ndi kuloza panyanja,+ kuti madzi abwerere ndi kumiza Aiguputo, magaleta awo ankhondo ndi asilikali awo apamahatchi.” Salimo 87:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ine ndidzatchula Rahabi*+ ndi Babulo+ monga ena mwa amene akundidziwa.Ponena za Filisitiya,+ Turo ndi Kusi ine ndidzati:“Amenewa anabadwira m’Ziyoni.”+ Yesaya 30:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Aiguputo ndi anthu achabechabe ndipo sadzakuthandizani chilichonse.+ Choncho ndinawatcha kuti, “Rahabi.+ Iwo sadzachita chilichonse.” Yesaya 51:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Dzuka! Dzuka! Vala mphamvu,+ iwe dzanja la Yehova!+ Dzuka ngati masiku akale, ngati m’mibadwo yakalekale.+ Kodi si iwe amene unaphwanyaphwanya Rahabi,+ amene unabaya* chilombo cha m’nyanja?+
26 Kenako Yehova anauza Mose kuti: “Tambasula dzanja lako ndi kuloza panyanja,+ kuti madzi abwerere ndi kumiza Aiguputo, magaleta awo ankhondo ndi asilikali awo apamahatchi.”
4 Ine ndidzatchula Rahabi*+ ndi Babulo+ monga ena mwa amene akundidziwa.Ponena za Filisitiya,+ Turo ndi Kusi ine ndidzati:“Amenewa anabadwira m’Ziyoni.”+
7 Aiguputo ndi anthu achabechabe ndipo sadzakuthandizani chilichonse.+ Choncho ndinawatcha kuti, “Rahabi.+ Iwo sadzachita chilichonse.”
9 Dzuka! Dzuka! Vala mphamvu,+ iwe dzanja la Yehova!+ Dzuka ngati masiku akale, ngati m’mibadwo yakalekale.+ Kodi si iwe amene unaphwanyaphwanya Rahabi,+ amene unabaya* chilombo cha m’nyanja?+