Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Lamulo limeneli laperekedwa kuti nsembe zimene ana a Isiraeli akuzipereka kunja,+ azibwera nazo kwa wansembe pakhomo la chihema chokumanako kuti azipereke kwa Yehova.+ Zimenezi ziziperekedwa monga nsembe zachiyanjano kwa Yehova.+

  • Yesaya 1:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Pakuti anthu adzachita manyazi ndi mitengo ikuluikulu imene inu munali kuilakalaka,+ ndipo mudzagwetsa nkhope zanu chifukwa cha minda imene mwasankha.+

  • Yesaya 66:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu amene akudzipatula ndi kudziyeretsa kuti apite kuminda+ n’kukaima kuseri kwa fano limene lili pakati pa mundawo, amene akudya nyama ya nkhumba+ ndi chinthu chonyansa, amene akudya ngakhale makoswe,+ onsewo adzathera limodzi,” akutero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena