-
Yeremiya 49:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 “‘Choncho taonani! Masiku adzafika,’ watero Yehova, ‘ndipo Raba,+ umene ndi mzinda wa ana a Amoni, ndidzaulizira chizindikiro chakuti kukubwera nkhondo.+ Ndipo mzindawu udzasanduka bwinja ndi mulu wadothi.+ Midzi yake yozungulira+ idzatenthedwa.’+
“‘Isiraeli adzatenga dziko la anthu amene analanda dziko lake,’+ watero Yehova.
-