2 Mafumu 23:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Kenako mfumuyo inagumula maguwa ansembe amene anali padenga la chipinda chapadenga+ cha Ahazi, amene mafumu a Yuda anamanga. Inagumulanso maguwa ansembe+ amene Manase anamanga pamabwalo awiri a nyumba ya Yehova. Itatero, inawaperapera komweko ndipo fumbi lake inakaliwaza kuchigwa* cha Kidironi. 2 Mafumu 23:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Inaphwanyaphwanya+ zipilala zopatulika ndipo inagwetsanso mizati yopatulika. Pamalo pamene panali zimenezi inadzazapo mafupa a anthu. Salimo 79:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 79 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowa m’dziko limene ndilo cholowa chanu.+Aipitsa kachisi wanu woyera.+Awononga Yerusalemu ndi kumusandutsa bwinja.+ Ezekieli 7:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Ndidzazipereka m’manja mwa alendo kuti zikhale zawo ndi kwa anthu oipa a padziko lapansi kuti azitenge,+ ndipo adzaziipitsa.
12 Kenako mfumuyo inagumula maguwa ansembe amene anali padenga la chipinda chapadenga+ cha Ahazi, amene mafumu a Yuda anamanga. Inagumulanso maguwa ansembe+ amene Manase anamanga pamabwalo awiri a nyumba ya Yehova. Itatero, inawaperapera komweko ndipo fumbi lake inakaliwaza kuchigwa* cha Kidironi.
14 Inaphwanyaphwanya+ zipilala zopatulika ndipo inagwetsanso mizati yopatulika. Pamalo pamene panali zimenezi inadzazapo mafupa a anthu.
79 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowa m’dziko limene ndilo cholowa chanu.+Aipitsa kachisi wanu woyera.+Awononga Yerusalemu ndi kumusandutsa bwinja.+
21 Ndidzazipereka m’manja mwa alendo kuti zikhale zawo ndi kwa anthu oipa a padziko lapansi kuti azitenge,+ ndipo adzaziipitsa.