Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno Hagara anayamba kutchula dzina la Yehova n’kunena kuti: “Inu ndinu Mulungu amene amaona chilichonse.”*+ Anatinso: “Kodi nanenso pano ndaona wotha kundionayo?”

  • Salimo 90:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Zolakwa zathu mwaziika patsogolo panu,+

      Ndipo machimo athu obisika* ali patsogolo pa nkhope yanu yowala.+

  • Salimo 139:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndingapite kuti kuthawa mzimu wanu,+

      Ndipo ndingapite kuti kuthawa nkhope yanu?+

  • Miyambo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Maso a Yehova ali paliponse.+ Amayang’ana anthu oipa ndi abwino omwe.+

  • Amosi 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Akakumba Manda* kuti abisale mmenemo ndidzawatulutsa ndi dzanja langa,+ ndipo akakwera kumwamba ndidzawatsitsira pansi.+

  • Aheberi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Palibe cholengedwa chimene Mulungu sangathe kuchiona.+ Chifukwa kwa iye zinthu zonse zili poonekera ndipo amatha kuziona bwinobwino. Ndipotu ife tikuyenera kudzayankha pa zochita zathu kwa Mulungu amene amaona zonseyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena