Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti maso ake amayang’anitsitsa njira za munthu,+

      Ndipo amaona mayendedwe ake onse.

  • Salimo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova ali m’kachisi wake wopatulika.+

      Yehova, mpando wake wachifumu uli kumwamba.+

      Maso ake amaona, maso ake owala amasanthula+ ana a anthu.

  • Salimo 66:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye akulamulira ndi mphamvu zake mpaka kalekale.+

      Maso ake akuyang’anitsitsa mitundu ya anthu.+

      Koma anthu oumitsa khosi asadzikweze.+ [Seʹlah.]

  • Miyambo 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti njira za munthu zili pamaso pa Yehova,+ ndipo iye amaonetsetsa njira zake zonse.+

  • Yeremiya 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti maso anga akuona njira zawo zonse. Anthuwo sanabisike kwa ine, ndipo zolakwa zawo sizinabisike pamaso panga.+

  • Yeremiya 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Kodi munthu aliyense angabisale m’malo obisika ine osamuona?”+ watero Yehova.

      “Kodi kumwamba kapena padziko lapansi, pali chilichonse chimene chingabisike kwa ine?”+ watero Yehova.

  • Aheberi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Palibe cholengedwa chimene Mulungu sangathe kuchiona.+ Chifukwa kwa iye zinthu zonse zili poonekera ndipo amatha kuziona bwinobwino. Ndipotu ife tikuyenera kudzayankha pa zochita zathu kwa Mulungu amene amaona zonseyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena