-
Ezekieli 29:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 “Iwe mwana wa munthu, Nebukadirezara+ mfumu ya Babulo anatuma gulu lake lankhondo kukachita utumiki wofunika kwambiri pomenyana ndi Turo.+ Mutu wa msilikali aliyense unameteka ndipo mapewa awo ananyuka.+ Koma mfumuyo ndi gulu lake lankhondo sanalandire cholowa+ chilichonse pa utumiki umene anachita pomenyana ndi Turo.
-