Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 N’chifukwa chake ndidzalirire mtengo wa mpesa wa ku Sibima ngati mmene ndinachitira polirira Yazeri.+ Ndidzakunyowetsa kwambiri ndi misozi yanga iwe Hesiboni+ ndi Eleyale,+ chifukwa chakuti kufuula kwakugwera m’chilimwe ndi pa nthawi ya zokolola zako.+

  • Yeremiya 48:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Kusangalala ndi kukondwera zachotsedwa m’munda wa zipatso ndiponso m’dziko la Mowabu.+ Ndachititsa kuti vinyo asapezeke moponderamo mphesa.+ Palibe amene adzapondaponda mphesa akufuula mosangalala. Padzamveka kufuula koma osati kwachisangalalo.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena