Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Pambuyo pake, Yakobo anaitana ana ake n’kuwauza kuti: “Sonkhanani pamodzi kuti ndikuuzeni zimene zidzachitika kwa inu m’masiku am’tsogolo.

  • Yeremiya 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mkwiyo wa Yehova sudzatha kufikira atachita zofuna za mtima wake+ ndi kuzikwaniritsa.+ M’masiku otsiriza, anthu inu mudzalingalira zimenezi ndipo mudzazimvetsa.+

  • Ezekieli 38:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “‘“Pakapita masiku ambiri, ine ndidzatembenukira kwa iwe. Pakatha zaka zambiri, iwe udzapita kudziko+ la anthu amene anapulumutsidwa ku lupanga ndi kubwerera kwawo. Udzapita kudziko la anthu amene anasonkhanitsidwa pamodzi kuchokera ku mitundu ina ya anthu+ n’kukakhala kumapiri a ku Isiraeli. Dziko lawo linali kuwonongedwa nthawi zonse ndipo tsopano muli anthu amene anachokera m’mayiko a anthu a mitundu ina. Onsewo akukhala m’dzikoli mwabata.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena