Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 31:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo iye anawafunsa kuti: “Kodi akazi onse mwawasiya amoyo?+

  • Oweruza 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mngelo wa Yehova+ anati: ‘Tembererani+ Merozi,

      Tembererani anthu ake mosaleka,

      Chifukwa sanathandize Yehova,

      Sanabwere ndi anthu amphamvu kudzathandiza Yehova.’

  • 1 Samueli 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiye n’chifukwa chiyani sunamvere mawu a Yehova, koma unathamangira zofunkha mosusuka+ ndi kuyamba kuchita zinthu zoipa pamaso pa Yehova?”+

  • 1 Mafumu 20:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Tsopano mneneriyo anauza mfumuyo kuti: “Yehova wanena kuti, ‘Popeza wamasula munthu woyenera kuwonongedwa ndi ine,+ moyo wako ulowa m’malo mwake+ ndipo anthu ako alowa m’malo mwa anthu ake.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena