Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 27:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Munthu aliyense woperekedwa kwa Mulungu kuti awonongedwe sangathe kuwomboledwa.+ Ameneyo aziphedwa ndithu.+

  • Yoswa 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma zinthu zoyenera kuwonongedwa musamale nazo,+ kuopera kuti mungazikhumbire+ n’kutengako zinthuzo,+ n’kuchititsa msasa wa Isiraeli nawonso kukhala chinthu choyenera kuwonongedwa ndi kunyanyalidwa.+

  • 1 Samueli 15:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma Sauli ndi anthu ake anamvera chisoni Agagi ndipo sanaphe nkhosa ndi ng’ombe zabwino kwambiri,+ ziweto zonenepa, nkhosa zamphongo ndi zina zonse zimene zinali zabwino. Iwo sanafune kupha zimenezi,+ koma anawononga zinthu zina zonse zimene zinali zonyansa ndi zonyozeka.

  • 1 Mbiri 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mwana wa Karami+ anali Akari,* amene anachititsa Isiraeli kunyanyalidwa.+ Iye anachita zinthu zosakhulupirika zokhudzana ndi chinthu choyenera kuwonongedwa.+

  • Yeremiya 48:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Wotembereredwa ndi munthu wozengereza kugwira ntchito imene Yehova wamupatsa.+ Wotembereredwa ndi munthu wopewa kukhetsa magazi ndi lupanga lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena