Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mbuzi yamphongoyo inali kudzitama mopitirira muyezo,+ koma itangokhala yamphamvu, nyanga yake yaikulu inathyoledwa. Pamalo pake panamera nyanga zinayi zoonekera patali zoloza kumphepo zinayi zakumwamba.+

  • Danieli 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mfumuyo ikadzauka,+ ufumu wake udzasweka ndipo udzagawanika ndi kutengedwa ndi mphepo zinayi+ zakumwamba,+ koma sudzapita kwa mbadwa zake+ ndipo maufumuwo sadzafanana ndi ufumu wake. Zimenezi zidzachitika chifukwa ufumu wake udzazulidwa ndi kuperekedwa kwa ena.

  • Chivumbulutso 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zimenezi zitatha, ndinaona angelo+ anayi ataimirira m’makona anayi a dziko lapansi. Iwo anali atagwira mwamphamvu mphepo zinayi+ za dziko lapansi, kuti mphepo iliyonse isawombe padziko lapansi, panyanja, kapena pamtengo uliwonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena