Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “‘Ndinadutsa pafupi nawe n’kukuona, ndipo ndinaona kuti inali nthawi yako yoti uchite zachikondi.+ Chotero ndinakuphimba ndi chovala changa+ ndipo ndinabisa maliseche ako. Ndinakulumbirira n’kuchita nawe pangano+ ndipo unakhala wanga,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.

  • Hoseya 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuyambira nthawi imeneyo mpaka m’tsogolo ndidzamupatsa minda yake ya mpesa.+ Ndidzamupatsanso chigwa cha Akori+ kuti chikhale ngati khomo lachiyembekezo. Pamenepo adzayankha ngati mmene anali kuyankhira ali mtsikana,+ ngatinso mmene anayankhira pa tsiku limene anatuluka m’dziko la Iguputo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena