Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Usakhale ndi milungu ina iliyonse+ kupatulapo ine.*

  • Deuteronomo 32:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iwo anali kupereka nsembe kwa ziwanda, osati kwa Mulungu.+

      Anapereka nsembe kwa milungu imene sanaidziwe,+

      Milungu yatsopano yongobwera kumene,+

      Imene makolo anu akale sanaidziwe.

  • Oweruza 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anayamba kusankha milungu yatsopano.+

      Atatero m’pamene nkhondo inafika m’mizinda.+

      Panalibe chishango kapena mkondo waung’ono,

      Pakati pa anthu 40,000 mu Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena