Levitiko 18:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Mukapewa kuchita zimenezi, dziko silidzakusanzani chifukwa choliipitsa mmene lidzasanzira mitundu imene ikukhalamo musanafike inu.+ Levitiko 20:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 “‘Motero inu muzisunga malangizo anga onse+ ndi zigamulo zanga zonse,+ kuti dziko limene ndikukulowetsani kuti mukhalemo lisakusanzeni.+ Maliro 4:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Anthu akuwafuulira kuti: “Chokani! Ndinu odetsedwa!+ Chokani! Chokani! Musatikhudze!”+Ansembe ndi aneneriwo alibe pokhala+ ndipo akungoyendayenda.+ Anthu a mitundu ina akunena kuti: “Amenewa sapitiriza kukhala kuno.+ Mika 2:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Nyamukani,+ chokani chifukwa ano si malo opumulirako.+ Dzikoli liwonongedwa chifukwa chakuti ladetsedwa+ ndipo kuwonongedwako kukhala kopweteka.+
28 Mukapewa kuchita zimenezi, dziko silidzakusanzani chifukwa choliipitsa mmene lidzasanzira mitundu imene ikukhalamo musanafike inu.+
22 “‘Motero inu muzisunga malangizo anga onse+ ndi zigamulo zanga zonse,+ kuti dziko limene ndikukulowetsani kuti mukhalemo lisakusanzeni.+
15 Anthu akuwafuulira kuti: “Chokani! Ndinu odetsedwa!+ Chokani! Chokani! Musatikhudze!”+Ansembe ndi aneneriwo alibe pokhala+ ndipo akungoyendayenda.+ Anthu a mitundu ina akunena kuti: “Amenewa sapitiriza kukhala kuno.+
10 Nyamukani,+ chokani chifukwa ano si malo opumulirako.+ Dzikoli liwonongedwa chifukwa chakuti ladetsedwa+ ndipo kuwonongedwako kukhala kopweteka.+