Yeremiya 27:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Kenako, uzitumize kwa mfumu ya Edomu,+ mfumu ya Mowabu,+ mfumu ya ana a Amoni,+ mfumu ya Turo+ ndi mfumu ya Sidoni.+ Upatsire amithenga amene akubwera ku Yerusalemu kudzaonana ndi Zedekiya mfumu ya Yuda. Ezekieli 32:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 “‘Kumeneko n’kumene kuli Edomu,+ mafumu ake ndi atsogoleri ake onse. Amenewa anaikidwa m’manda akadali amphamvu. Anaikidwa pamodzi ndi ophedwa ndi lupanga.+ Iwo adzagona limodzi ndi anthu osadulidwa+ komanso anthu amene akutsikira kudzenje. Obadiya 1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 1 Tsopano awa ndiwo masomphenya a Obadiya: Zimene Yehova Ambuye Wamkulu Koposa wanena zokhudza Edomu ndi izi:+ “Ife tamva uthenga wochokera kwa Yehova ndipo nthumwi yatumidwa kwa anthu a mitundu ina kukanena kuti: ‘Nyamukani anthu inu, tiyeni timuukire ndi kumenyana naye.’”+
3 Kenako, uzitumize kwa mfumu ya Edomu,+ mfumu ya Mowabu,+ mfumu ya ana a Amoni,+ mfumu ya Turo+ ndi mfumu ya Sidoni.+ Upatsire amithenga amene akubwera ku Yerusalemu kudzaonana ndi Zedekiya mfumu ya Yuda.
29 “‘Kumeneko n’kumene kuli Edomu,+ mafumu ake ndi atsogoleri ake onse. Amenewa anaikidwa m’manda akadali amphamvu. Anaikidwa pamodzi ndi ophedwa ndi lupanga.+ Iwo adzagona limodzi ndi anthu osadulidwa+ komanso anthu amene akutsikira kudzenje.
1 Tsopano awa ndiwo masomphenya a Obadiya: Zimene Yehova Ambuye Wamkulu Koposa wanena zokhudza Edomu ndi izi:+ “Ife tamva uthenga wochokera kwa Yehova ndipo nthumwi yatumidwa kwa anthu a mitundu ina kukanena kuti: ‘Nyamukani anthu inu, tiyeni timuukire ndi kumenyana naye.’”+