Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “‘Musamadzicheke chifukwa cha munthu wakufa,+ ndipo musamadziteme zizindikiro. Ine ndine Yehova.

  • Deuteronomo 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu.+ Musamadzichekecheke+ kapena kumeta+ nsidze* zanu chifukwa cha anthu akufa.

  • Yeremiya 41:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 kunabwera amuna ochokera ku Sekemu,+ ku Silo+ ndi ku Samariya.+ Iwo analipo 80 ndipo anabwera atameta ndevu,+ atadzichekacheka ndiponso atang’amba zovala zawo.+ Amunawa anabwera ndi nsembe yambewu ndi lubani+ m’manja mwawo kuti adzazipereke kunyumba ya Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena