Levitiko 26:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Chotero adzavomereza kuti iwo komanso makolo awo anayenda motsutsana nane,+ anandichimwira+ ndi kundichitira mosakhulupirika. Nehemiya 1:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Mukadzabwerera kwa ine+ ndi kusunga malamulo anga,+ ngakhale anthu omwazikana a mtundu wanu atakhala kumalekezero a kumwamba, ndidzawasonkhanitsa kuchokera kumeneko+ ndi kuwabweretsa+ kumalo amene ndasankha kuikako dzina langa.’+ Ezekieli 16:61 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 61 Ndithu udzakumbukira njira zako+ ndipo udzachita manyazi ukadzalandira akulu ako ndi ang’ono ako. Ndidzawapereka kwa iwe ngati ana ako aakazi,+ koma osati chifukwa cha pangano limene ndinapangana nawe.’+ Hoseya 5:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Kenako ndidzabwerera kumalo anga kufikira iwo atalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo+ ndipo adzayamba kufunafuna nkhope yanga.+ Zinthu zikadzawavuta,+ adzandifuna.”+
40 Chotero adzavomereza kuti iwo komanso makolo awo anayenda motsutsana nane,+ anandichimwira+ ndi kundichitira mosakhulupirika.
9 Mukadzabwerera kwa ine+ ndi kusunga malamulo anga,+ ngakhale anthu omwazikana a mtundu wanu atakhala kumalekezero a kumwamba, ndidzawasonkhanitsa kuchokera kumeneko+ ndi kuwabweretsa+ kumalo amene ndasankha kuikako dzina langa.’+
61 Ndithu udzakumbukira njira zako+ ndipo udzachita manyazi ukadzalandira akulu ako ndi ang’ono ako. Ndidzawapereka kwa iwe ngati ana ako aakazi,+ koma osati chifukwa cha pangano limene ndinapangana nawe.’+
15 Kenako ndidzabwerera kumalo anga kufikira iwo atalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo+ ndipo adzayamba kufunafuna nkhope yanga.+ Zinthu zikadzawavuta,+ adzandifuna.”+