29 “Usasangalale+ iwe Filisitiya,+ kapena aliyense wokhala mwa iwe chifukwa chakuti ndodo ya amene anali kukumenya yathyoka.+ Pakuti pamuzu wa njokayo+ padzaphuka njoka yapoizoni,+ ndipo chipatso chake chidzakhala njoka yothamanga, yaululu wamoto.+
20 khamu lonse la anthu a mitundu yosiyanasiyana, mafumu onse a dziko la Uzi,+ mafumu onse a dziko la Afilisiti,+ Asikeloni,+ Gaza,+ Ekironi+ ndi otsala onse a ku Asidodi,+