Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 14:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Fuula chipata iwe! Lira mokweza mzinda iwe! Nonsenu mudzataya mtima, inu anthu okhala m’Filisitiya! Pakuti utsi ukubwera kuchokera kumpoto, ndipo palibe msilikali amene akutsalira pa magulu ake ankhondo.”+

  • Yeremiya 47:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Yehova anauza mneneri Yeremiya mawu okhudza Afilisiti.+ Pa nthawiyi, Farao anali asanathire nkhondo mzinda wa Gaza.+

  • Ezekieli 25:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Afilisiti achitira zoipa+ Aisiraeli ndipo akupitiriza kuwachitira zoipazo. Mumtima mwawo akusangalala ndiponso kuwanyoza. Akuchita zimenezi kuti awawononge+ chifukwa cha chidani chawo chomwe chidzakhalepo mpaka kalekale.+

  • Amosi 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndidzapha anthu a ku Asidodi+ pamodzi ndi wogwira ndodo yachifumu wa ku Asikeloni.+ Ndidzalanga+ Ekironi+ ndipo ndidzafafaniza otsala mwa Afilisiti,”+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’

  • Zefaniya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Tsoka kwa anthu okhala m’chigawo cha m’mphepete mwa nyanja, mtundu wa Akereti.+ Yehova wakudzudzulani anthu inu. Iwe Kanani, dziko la Afilisiti, nawenso ndidzakuwononga, kotero kuti m’dziko lako simudzatsala munthu aliyense.+

  • Zekariya 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mwana wochokera mu mtundu wina wa anthu+ adzakhala mu Asidodi,+ ndipo ine ndidzathetsa kunyada kwa Afilisiti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena