Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 31:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Amuna a Isiraeli amene anali m’dera la m’chigwa ndiponso m’dera la Yorodano ataona kuti asilikali a Isiraeli athawa komanso kuti Sauli ndi ana ake afa, anayamba kuchoka m’mizinda yawo ndi kuthawa.+ Kenaka Afilisiti anabwera n’kuyamba kukhala m’mizindayo.+

  • 2 Samueli 5:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsopano Afilisiti anamva kuti Davide amudzoza kukhala mfumu ya Isiraeli.+ Choncho Afilisiti onse anabwera kudzafunafuna Davide. Davide atamva zimenezi, anakabisala kumalo ovuta kufikako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena