Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 14:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “Usasangalale+ iwe Filisitiya,+ kapena aliyense wokhala mwa iwe chifukwa chakuti ndodo ya amene anali kukumenya yathyoka.+ Pakuti pamuzu wa njokayo+ padzaphuka njoka yapoizoni,+ ndipo chipatso chake chidzakhala njoka yothamanga, yaululu wamoto.+

  • Yeremiya 47:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo adzachita mantha chifukwa cha tsiku limene likubwera. Tsikuli ndi lofunkha zinthu za Afilisiti+ onse ndi kupha wopulumuka aliyense wothandiza+ Turo+ ndi Sidoni.+ Pakuti Yehova adzafunkha zinthu za Afilisiti+ amene atsala ochokera pachilumba cha Kafitori.+

  • Ezekieli 25:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Ine ndikutambasula dzanja langa kuti ndilange Afilisiti,+ ndipo ndidzapha Akereti+ ndi kuwononga anthu onse okhala m’mbali mwa nyanja.+

  • Zefaniya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Tsoka kwa anthu okhala m’chigawo cha m’mphepete mwa nyanja, mtundu wa Akereti.+ Yehova wakudzudzulani anthu inu. Iwe Kanani, dziko la Afilisiti, nawenso ndidzakuwononga, kotero kuti m’dziko lako simudzatsala munthu aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena