Yobu 34:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Choncho inu amuna a mtima+ womvetsa zinthu, ndimvereni.Mulungu woona sangachite zoipa m’pang’ono pomwe,+Ndipo Wamphamvuyonse sangachite zinthu zopanda chilungamo ngakhale pang’ono.+ Yobu 40:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Kodi ndithu ukuchititsa chilungamo changa kukhala chopanda pake?Kodi ukunena kuti ine ndine wolakwa kuti iweyo ukhale wolondola?+ Salimo 92:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Kuti alengeze kuti Yehova ndi wolungama.+Iye ndi Thanthwe langa,+ ndipo sachita zosalungama.+ Aroma 3:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ayi! Koma Mulungu akhale wonena zoona,+ ngakhale kuti munthu aliyense angapezeke kukhala wonama,+ monganso Malemba amanenera kuti: “Mukamalankhula mumalankhula zachilungamo, kuti mupambane pamene mukuweruzidwa.”+
10 Choncho inu amuna a mtima+ womvetsa zinthu, ndimvereni.Mulungu woona sangachite zoipa m’pang’ono pomwe,+Ndipo Wamphamvuyonse sangachite zinthu zopanda chilungamo ngakhale pang’ono.+
8 Kodi ndithu ukuchititsa chilungamo changa kukhala chopanda pake?Kodi ukunena kuti ine ndine wolakwa kuti iweyo ukhale wolondola?+
4 Ayi! Koma Mulungu akhale wonena zoona,+ ngakhale kuti munthu aliyense angapezeke kukhala wonama,+ monganso Malemba amanenera kuti: “Mukamalankhula mumalankhula zachilungamo, kuti mupambane pamene mukuweruzidwa.”+