Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho inu amuna a mtima+ womvetsa zinthu, ndimvereni.

      Mulungu woona sangachite zoipa m’pang’ono pomwe,+

      Ndipo Wamphamvuyonse sangachite zinthu zopanda chilungamo ngakhale pang’ono.+

  • Yobu 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kodi ndithu ukuchititsa chilungamo changa kukhala chopanda pake?

      Kodi ukunena kuti ine ndine wolakwa kuti iweyo ukhale wolondola?+

  • Salimo 92:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuti alengeze kuti Yehova ndi wolungama.+

      Iye ndi Thanthwe langa,+ ndipo sachita zosalungama.+

  • Aroma 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ayi! Koma Mulungu akhale wonena zoona,+ ngakhale kuti munthu aliyense angapezeke kukhala wonama,+ monganso Malemba amanenera kuti: “Mukamalankhula mumalankhula zachilungamo, kuti mupambane pamene mukuweruzidwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena