Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “‘Muzisunga masabata anga+ ndipo muziopa malo anga opatulika.+ Ine ndine Yehova.

  • Levitiko 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ine ndidzam’kana* munthu ameneyo, ndipo ndidzamupha kuti asakhalenso pakati pa anthu amtundu wake,+ chifukwa wapereka mwana wake kwa Moleki kuti aipitse malo anga oyera+ ndi kuipitsa dzina langa loyera.+

  • 2 Mafumu 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komanso iye anaika m’nyumbayo chifaniziro+ cha mzati wopatulika chimene anapanga. Koma ponena za nyumba imeneyo,+ Yehova anauza Davide ndi Solomo mwana wake kuti: “M’nyumba iyi ndiponso mu Yerusalemu mzinda umene ndausankha pa mafuko onse a Isiraeli, ndidzaikamo dzina langa mpaka kalekale.+

  • 2 Mbiri 36:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Komanso, anthu ndi atsogoleri onse a ansembe+ anachita zosakhulupirika zochuluka kwambiri mofanana ndi zonyansa zonse+ za anthu a mitundu ina. Choncho iwo anaipitsa nyumba ya Yehova imene iye anaiyeretsa ku Yerusalemu.+

  • Yeremiya 32:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Iwo anaika zinthu zawo zonyansa m’nyumba imene imatchedwa ndi dzina langa kuti aiipitse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena