Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Chifukwa kundipsera mtima kwako+ ndi kufuula kwako zafika m’makutu mwanga,+

      Ndithu ndidzakola mphuno yako ndi ngowe yanga, ndipo ndidzamanga zingwe zanga pakamwa pako.+

      Kenako ndidzakukoka n’kukubweza kudzera njira imene unadutsa pobwera.”+

  • Ezekieli 29:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndidzakukola ndi ngowe munsagwada zako+ ndi kuchititsa nsomba za m’ngalande za mtsinje wa Nailo kukakamira kumamba ako. Ndidzakutulutsa m’ngalande za Nailo pamodzi ndi nsomba zonse za m’ngalandezo zimene zakakamira kumamba ako.

  • Ezekieli 39:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndidzakubweza ndi kukutsogolera.+ Ndidzakutenga kuchokera kumadera akutali kwambiri a kumpoto,+ n’kukubweretsa kumapiri a ku Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena