-
Yeremiya 30:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 “Koma iwe Yakobo mtumiki wanga usachite mantha, iwe Isiraeli usagwidwe ndi mantha,”+ watero Yehova. “Pakuti ine ndikukupulumutsa kuchokera kutali ndipo ndikupulumutsanso ana ako kuchokera kudziko limene anatengedwa kukakhala akapolo.+ Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala mosatekeseka komanso mopanda zosokoneza. Sipadzakhala womuopsa.”+
-
-
Ezekieli 14:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Koma ndithu m’dzikolo mudzatsala kagulu ka anthu amene adzapulumuke ndipo adzatulutsidwamo.+ Taonani ana aamuna ndi aakazi! Iwo akubwera kwa inu, ndipo mudzaona njira yawo ndi zochita zawo.+ Inu mudzatonthozedwa pambuyo pa tsoka limene ndidzabweretse pa Yerusalemu, ngakhalenso pambuyo pa zonse zimene ndidzabweretsere mzindawo.’”
-