Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 32:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma mukapanda kuchita zimenezo, ndithu mudzachimwira Yehova.+ Ndipo mukatero, dziwani kuti tchimo lanu lidzakutsatani.+

  • Yeremiya 40:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehova ananena za tsoka limeneli moti anatsimikiza kukwaniritsa zimene ananenazo. Anatero chifukwa anthu inu munachimwira Yehova ndipo simunamvere mawu ake. Choncho monga mmene ukuoneramu, zimenezi zachitikadi.+

  • Ezekieli 18:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “‘Chotero ine ndidzaweruza aliyense wa inu malinga ndi njira zake,+ inu a nyumba ya Isiraeli,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.+ ‘Lapani ndi kusiya zolakwa zanu zonse+ ndipo musalole kuti chilichonse chizikupunthwitsani ndi kukulakwitsani.+

  • Ezekieli 33:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Anthu inu mwanena kuti, ‘Njira za Yehova n’zopanda chilungamo.’+ Inu a nyumba ya Isiraeli, ine ndidzaweruza aliyense wa inu malinga ndi njira zake.”+

  • Aroma 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye adzaweruza aliyense malinga ndi ntchito zake motere:+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena