Miyambo 19:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Kupusa kwa munthu wochokera kufumbi n’kumene kumapotoza njira yake,+ choncho mtima wake umakwiyira Yehova.+ Yesaya 55:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 “Maganizo a anthu inu si maganizo anga,+ ndipo njira zanga si njira zanu,”+ akutero Yehova. Yesaya 55:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Pakuti monga momwe kumwamba kulili pamwamba kuposa dziko lapansi,+ momwemonso njira zanga n’zapamwamba kuposa njira zanu,+ ndiponso maganizo anga ndi apamwamba kuposa maganizo anu.+ Ezekieli 18:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 “‘Anthu inu mudzanena kuti: “Njira za Yehova n’zopanda chilungamo.”+ Tamverani inu a nyumba ya Isiraeli. Kodi njira zanga ndiye zopanda chilungamo?+ Kodi njira za anthu inu sindizo zopanda chilungamo?+ Ezekieli 18:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 “‘Ndithu nyumba ya Isiraeli idzanena kuti: “Njira za Yehova n’zopanda chilungamo.”+ Kodi njira zanga ndiye zopanda chilungamo, inu a nyumba ya Isiraeli?+ Kodi njira za anthu inu sindizo zopanda chilungamo?’+
3 Kupusa kwa munthu wochokera kufumbi n’kumene kumapotoza njira yake,+ choncho mtima wake umakwiyira Yehova.+
9 “Pakuti monga momwe kumwamba kulili pamwamba kuposa dziko lapansi,+ momwemonso njira zanga n’zapamwamba kuposa njira zanu,+ ndiponso maganizo anga ndi apamwamba kuposa maganizo anu.+
25 “‘Anthu inu mudzanena kuti: “Njira za Yehova n’zopanda chilungamo.”+ Tamverani inu a nyumba ya Isiraeli. Kodi njira zanga ndiye zopanda chilungamo?+ Kodi njira za anthu inu sindizo zopanda chilungamo?+
29 “‘Ndithu nyumba ya Isiraeli idzanena kuti: “Njira za Yehova n’zopanda chilungamo.”+ Kodi njira zanga ndiye zopanda chilungamo, inu a nyumba ya Isiraeli?+ Kodi njira za anthu inu sindizo zopanda chilungamo?’+