Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Iwe mwana wa munthu, amuna awa aika mitima yawo pamafano onyansa, ndipo aika pamaso pawo chinthu chopunthwitsa chimene chimawalakwitsa.+ Kodi ndiwayankhe iwo akamandifunsa?+

  • Ezekieli 44:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ine ndatambasula dzanja langa kuti ndiwalange+ chifukwa chakuti anali kutumikira anthu pamaso pa mafano awo onyansa.+ Iwo anakhala chopunthwitsa kwa anthu a nyumba ya Isiraeli ndipo anawachititsa zinthu zoipa,+ choncho adzakumana ndi zotsatira za zochita zawo,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena