Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamenepo Yehova akamapita kukapha Aiguputo ndi mliri, akaona magazi pamafelemu a pamwamba pa zitseko zanu ndi mafelemu awiri a m’mbali mwa khomo, Yehova adzapitirira khomo limenelo ndipo sadzalola chiwonongeko kulowa m’nyumba zanu ndi kukuphani.+

  • Yoswa 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Tikubwera ndithu m’dziko muno! Chingwe chofiira ichi uchimangirire pawindo limene watitulutsirapo. Bambo ako ndi mayi ako, abale ako ndi alongo ako, ndi onse a m’nyumba ya bambo ako, uwasonkhanitse kuti adzakhale m’nyumba mwako.+

  • Chivumbulutso 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndipo linauzidwa kuti lisawononge zomera za padziko lapansi, kapena chilichonse chobiriwira, kapena mtengo uliwonse, koma livulaze anthu okhawo amene alibe chidindo cha Mulungu pamphumi pawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena