Nehemiya 2:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamenepo ndinayankha mfumuyo kuti: “Mfumu ikhale ndi moyo wautali!+ Kodi nkhope yanga ilekerenji kukhala yachisoni pamene mzinda+ umene makolo anga+ anaikidwako uli bwinja ndipo zipata zake zinatenthedwa ndi moto?”+ Danieli 2:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Pamenepo Akasidi anayankha mfumu m’chinenero cha Chiaramu+ kuti: “Inu mfumu mukhale ndi moyo mpaka kalekale.*+ Tiuzeni ife atumiki anu zimene mwalota ndipo tikumasulirani malotowo.”+ Danieli 5:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tsopano popeza mfumukazi inamva mawu a mfumu ndi a nduna zake, inalowa m’chipinda chimene anali kuchitira phwandolo. Mfumukaziyo inati: “Inu mfumu, mukhale ndi moyo mpaka kalekale.+ Musachite mantha komanso nkhope yanu isasinthe.
3 Pamenepo ndinayankha mfumuyo kuti: “Mfumu ikhale ndi moyo wautali!+ Kodi nkhope yanga ilekerenji kukhala yachisoni pamene mzinda+ umene makolo anga+ anaikidwako uli bwinja ndipo zipata zake zinatenthedwa ndi moto?”+
4 Pamenepo Akasidi anayankha mfumu m’chinenero cha Chiaramu+ kuti: “Inu mfumu mukhale ndi moyo mpaka kalekale.*+ Tiuzeni ife atumiki anu zimene mwalota ndipo tikumasulirani malotowo.”+
10 Tsopano popeza mfumukazi inamva mawu a mfumu ndi a nduna zake, inalowa m’chipinda chimene anali kuchitira phwandolo. Mfumukaziyo inati: “Inu mfumu, mukhale ndi moyo mpaka kalekale.+ Musachite mantha komanso nkhope yanu isasinthe.