Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 121:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 121 Ndakweza maso anga kuyang’ana kumapiri.+

      Kodi thandizo langa lichokera kuti?+

  • Salimo 123:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 123 Ndakweza maso anga kuyang’ana inu,+

      Kuyang’ana inu amene mukukhala kumwamba.+

  • Salimo 123:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Taonani! Monga mmene maso a atumiki amayang’anira dzanja la mbuye wawo,+

      Mmene maso a kapolo wamkazi amayang’anira dzanja la mbuye wake wamkazi,+

      Momwemonso, maso athu adzayang’ana kwa Yehova Mulungu wathu,+

      Kufikira atatikomera mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena