Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:100
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 100 Ndimachita zinthu mozindikira kuposa anthu achikulire,+

      Chifukwa ndimasunga malamulo anu.+

  • Miyambo 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Nzeru ndiyo chinthu chofunika kwambiri.+ Peza nzeru, ndipo pa zinthu zonse zimene upeze, upezenso luso lomvetsa zinthu.+

  • Miyambo 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Uzilemekeze kwambiri ndipo zidzakukweza.+ Zidzakulemekeza chifukwa chakuti wazikumbatira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena