Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Ine ndine Yehova Mulungu wako,+ amene ndinakutulutsa m’dziko la Iguputo, m’nyumba yaukapolo.+

  • Levitiko 11:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Ine ndine Yehova amene ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo kuti ndikusonyezeni kuti ndine Mulungu.+ Muzikhala oyera,+ chifukwa ine ndine woyera.+

  • Salimo 81:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ine Yehova, ndine Mulungu wanu,+

      Amene ndinakutulutsani m’dziko la Iguputo.+

      Tsegulani pakamwa panu ndipo ndidzaikamo chakudya.+

  • Hoseya 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Ine ndine Yehova Mulungu wako kuchokera pamene unali ku Iguputo.+ Koma ndidzakuchititsa kukhala m’mahema ngati pa masiku achikondwerero.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena