Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Udzalimadi ndi kubzala mitengo ya mpesa, koma sudzakolola mphesa zake ndi kumwa vinyo,+ chifukwa mbozi zidzadya mpesawo.+

  • Yesaya 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Vinyo watsopano akulira, ndipo mtengo wa mpesa wafota.+ Anthu onse amene anali kusangalala mumtima mwawo akuusa moyo.+

  • Hoseya 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Malo opunthira mbewu ndiponso oponderamo mphesa sakukupatsa chakudya,+ ndipo vinyo wotsekemera akukukhumudwitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena