Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kukondwera ndi kusangalala zachotsedwa m’munda wako wa zipatso, ndipo m’minda ya mpesa mulibe mfuu yachisangalalo. Mulibe aliyense amene akufuula.+ Mopondera mphesa mulibe amene akuponda vinyo.+ Ndachititsa kuti kufuula kulekeke.+

  • Yesaya 32:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Dzimenyeni pachifuwa pomva chisoni+ chifukwa cha kuwonongeka kwa minda yachonde+ ndi minda ya mpesa.

  • Amosi 5:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ‘Padzakhala kulira mokweza m’minda yonse ya mpesa+ pakuti ine ndidzadutsa pakati panu,’+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena