Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 24:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nyimbo zachisangalalo zoimbidwa ndi maseche zasiya kumveka. Phokoso la anthu okondwa kwambiri silikumvekanso. Nyimbo zachisangalalo zoimbidwa ndi zeze zaleka kumveka.+

  • Yeremiya 25:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Ndiyeno iweyo, unenere mawu onsewa, ndipo anthuwo uwauze kuti, ‘Yehova adzabangula ngati mkango ali kumwamba,+ ndipo adzafuula ali kumalo ake oyera kumene amakhala.+ Iye adzabanguliradi malo ake okhalapo a padziko lapansi. Adzaimbira anthu onse okhala padziko lapansi nyimbo yofanana ndi imene anthu oponda mphesa amaimba.’+

  • Yeremiya 48:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Kusangalala ndi kukondwera zachotsedwa m’munda wa zipatso ndiponso m’dziko la Mowabu.+ Ndachititsa kuti vinyo asapezeke moponderamo mphesa.+ Palibe amene adzapondaponda mphesa akufuula mosangalala. Padzamveka kufuula koma osati kwachisangalalo.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena