Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pambuyo pake, Azariya anagona pamodzi ndi makolo ake+ ndipo anamuika m’manda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide. Kenako Yotamu mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake.+

  • 2 Mafumu 15:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 M’chaka chachiwiri cha Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Isiraeli, Yotamu+ mwana wa Uziya+ mfumu ya Yuda anakhala mfumu.

  • 1 Mbiri 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehoasi anabereka Amaziya,+ Amaziya anabereka Azariya,+ Azariya anabereka Yotamu,+

  • 2 Mbiri 27:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yotamu+ anali ndi zaka 25 pamene anayamba kulamulira, ndipo analamulira ku Yerusalemu zaka 16. Mayi ake dzina lawo linali Yerusa+ mwana wa Zadoki.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena