Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 14:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndidzathyola Msuri amene ali m’dziko langa+ ndipo ndidzamupondaponda pamapiri anga.+ Goli lake lidzachoka pa iwo ndipo katundu wake adzachoka pamapewa awo.”+

  • Yeremiya 30:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Pa tsikuli ndidzathyola goli ndi kulichotsa m’khosi lanu. Ndidzadula zingwe zimene akumangani nazo,+ moti alendowo sadzagwiritsanso ntchito Yakobo monga wantchito wawo,” watero Yehova wa makamu.

  • Hoseya 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndinali kuwakoka mokoma mtima ndi mwachikondi,*+ moti kwa iwo ndinakhala ngati wochotsa goli m’khosi*+ mwawo ndipo mwachikondi ndinali kubweretsera aliyense wa iwo chakudya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena