Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 30:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Chifukwa cha mawu a Yehova, dziko la Asuri lidzagwidwa ndi mantha,+ ndipo iye adzalimenya ndi ndodo.+

  • Yesaya 31:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Msuri adzaphedwa ndi lupanga, koma osati la munthu. Lupanga lidzamudya, koma osati la munthu wochokera kufumbi.+ Iye adzathawa chifukwa cha lupangalo ndipo ana ake aamuna adzagwiritsidwa ntchito yaukapolo.

  • Yesaya 37:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Choncho Senakeribu+ mfumu ya Asuri anachokako n’kubwerera+ kukakhala ku Nineve.+

  • Ezekieli 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Wafanana ndi Msuri. Wafanana ndi mtengo wa mkungudza wa ku Lebanoni,+ wanthambi zikuluzikulu zokongola,+ wanthambi za masamba ambiri zopereka mthunzi, mtengo wautali kwambiri+ umene nsonga yake inafika m’mitambo.+

  • Ezekieli 32:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kumeneko n’kumene kuli Asuri ndi khamu lake lonse.+ Manda a anthu a ku Asuri ali mozungulira mfumu yawo. Onsewo anaphedwa ndi lupanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena