Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 42:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Ndadziwa kuti inu mumatha kuchita zinthu zonse,+

      Ndipo palibe zimene simungakwanitse.+

  • Yeremiya 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu onse.+ Kodi kwa ine pali nkhani ina iliyonse yovuta?+

  • Maliko 10:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yesu anawayang’ana ndi kuwauza kuti: “Kwa anthu n’zosathekadi, koma sizili choncho kwa Mulungu, pakuti zinthu zonse n’zotheka ndi Mulungu.”+

  • Luka 18:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iye anawauza kuti: “Zinthu zosatheka ndi anthu n’zotheka ndi Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena