Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Patapita nthawi, mfumu ndi anthu ake anapita ku Yerusalemu kukamenyana ndi Ayebusi+ amene anali kukhala kumeneko. Ayebusiwo anayamba kuuza Davide kuti: “Sulowa mumzinda uno, pakuti upitikitsidwa ndi anthu akhungu ndi olumala.”+ Mumtima mwawo iwo anali kunena kuti: “Davide sangalowe mumzinda uno.”

  • 1 Mafumu 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu onse otsala a Aamori,+ Ahiti,+ Aperezi,+ Ahivi,+ ndi Ayebusi,+ amene sanali ana a Isiraeli,+

  • 1 Mbiri 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pambuyo pake Davide ndi Aisiraeli onse anapita ku Yerusalemu,+ kapena kuti ku Yebusi,+ dziko limene kunali kukhala Ayebusi.+

  • 1 Mbiri 21:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Davide ataona kuti Yehova wamuyankha pamalo opunthira mbewu a Orinani Myebusi, anapitiriza kuperekera nsembe pamalopo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena