-
Yobu 26:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Iye anatambasula kumpoto pamwamba pa malo opanda kanthu,+
Ndipo anakoloweka dziko lapansi m’malere.
-
Salimo 104:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Mwadzifunditsa kuwala ngati chofunda,+
Mwatambasula kumwamba ngati nsalu ya chihema.+
-
-
-