Luka 21:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “Koma zonsezi zisanachitike, anthu adzakugwirani ndi kukuzunzani,+ adzakuperekani kumasunagoge ndi kundende. Adzakutengerani kwa mafumu ndi abwanamkubwa chifukwa cha dzina langa.+ Yohane 16:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Anthu adzakuchotsani m’sunagoge.+ Ndipo nthawi ikubwera pamene aliyense wakupha inu adzaganiza kuti wachita utumiki wopatulika kwa Mulungu.+ Machitidwe 5:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Pamenepo iwo anamvera mawu ake, ndipo anaitanitsa atumwiwo. Ndiyeno anangowakwapula+ ndi kuwalamula kuti asiye kulankhula m’dzina la Yesu,+ kenako anawamasula. 2 Akorinto 11:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kasanu Ayuda anandikwapula zikoti 40+ kuchotsera chimodzi. 1 Atesalonika 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 amene anapha ngakhale Ambuye Yesu+ ndi aneneri+ ndi kuzunzanso ifeyo.+ Ndipo iwo sakukondweretsa Mulungu, koma akutsekereza zinthu zopindulitsa anthu onse.
12 “Koma zonsezi zisanachitike, anthu adzakugwirani ndi kukuzunzani,+ adzakuperekani kumasunagoge ndi kundende. Adzakutengerani kwa mafumu ndi abwanamkubwa chifukwa cha dzina langa.+
2 Anthu adzakuchotsani m’sunagoge.+ Ndipo nthawi ikubwera pamene aliyense wakupha inu adzaganiza kuti wachita utumiki wopatulika kwa Mulungu.+
40 Pamenepo iwo anamvera mawu ake, ndipo anaitanitsa atumwiwo. Ndiyeno anangowakwapula+ ndi kuwalamula kuti asiye kulankhula m’dzina la Yesu,+ kenako anawamasula.
15 amene anapha ngakhale Ambuye Yesu+ ndi aneneri+ ndi kuzunzanso ifeyo.+ Ndipo iwo sakukondweretsa Mulungu, koma akutsekereza zinthu zopindulitsa anthu onse.