Deuteronomo 19:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 kuti musakhetse magazi a munthu wosalakwa+ pakati pa dziko lanu limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, kotero kuti musakhale ndi mlandu wa magazi.+ Yoswa 2:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Aliyense amene adzatuluke pakhomo la nyumba yako kupita panja,+ magazi ake adzakhala pamutu pake. Ife tidzakhala opanda mlandu. Koma ngati aliyense amene adzakhalebe limodzi nawe m’nyumbamu adzaphedwe, magazi ake adzakhale pamutu pathu. Machitidwe 5:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 kuti: “Tinakulamulani mwamphamvu+ kuti musadzaphunzitsenso m’dzina limeneli, koma taonani tsopano! Mwadzaza Yerusalemu yense ndi chiphunzitso chanuchi,+ ndipo mwatsimikiza mtima ndithu kuti mubweretse magazi+ a munthu ameneyu pa ife.” 1 Atesalonika 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 amene anapha ngakhale Ambuye Yesu+ ndi aneneri+ ndi kuzunzanso ifeyo.+ Ndipo iwo sakukondweretsa Mulungu, koma akutsekereza zinthu zopindulitsa anthu onse.
10 kuti musakhetse magazi a munthu wosalakwa+ pakati pa dziko lanu limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani monga cholowa, kotero kuti musakhale ndi mlandu wa magazi.+
19 Aliyense amene adzatuluke pakhomo la nyumba yako kupita panja,+ magazi ake adzakhala pamutu pake. Ife tidzakhala opanda mlandu. Koma ngati aliyense amene adzakhalebe limodzi nawe m’nyumbamu adzaphedwe, magazi ake adzakhale pamutu pathu.
28 kuti: “Tinakulamulani mwamphamvu+ kuti musadzaphunzitsenso m’dzina limeneli, koma taonani tsopano! Mwadzaza Yerusalemu yense ndi chiphunzitso chanuchi,+ ndipo mwatsimikiza mtima ndithu kuti mubweretse magazi+ a munthu ameneyu pa ife.”
15 amene anapha ngakhale Ambuye Yesu+ ndi aneneri+ ndi kuzunzanso ifeyo.+ Ndipo iwo sakukondweretsa Mulungu, koma akutsekereza zinthu zopindulitsa anthu onse.