Mateyu 10:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mayina a atumwi 12+ aja ndi awa:+ Simoni, wotchedwa Petulo,*+ ndi Andireya+ m’bale wake. Yakobo mwana wa Zebedayo+ ndi m’bale wake Yohane. Mateyu 27:56 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 56 Pakati pawo panali Mariya Mmagadala, Mariya mayi a Yakobo ndi Yose, ndiponso panali mayi a Yakobo ndi Yohane.*+ Maliko 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Yakobo mwana wa Zebedayo, Yohane m’bale wa Yakobo+ (awiriwa anawatchanso a Boanege, kutanthauza Ana a Bingu), Maliko 10:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Koma Yakobo ndi Yohane, ana aamuna awiri a Zebedayo,+ anapita kwa iye ndi kumuuza kuti: “Mphunzitsi, tikufuna mutichitire chimene tikupempheni.”+
2 Mayina a atumwi 12+ aja ndi awa:+ Simoni, wotchedwa Petulo,*+ ndi Andireya+ m’bale wake. Yakobo mwana wa Zebedayo+ ndi m’bale wake Yohane.
56 Pakati pawo panali Mariya Mmagadala, Mariya mayi a Yakobo ndi Yose, ndiponso panali mayi a Yakobo ndi Yohane.*+
17 Yakobo mwana wa Zebedayo, Yohane m’bale wa Yakobo+ (awiriwa anawatchanso a Boanege, kutanthauza Ana a Bingu),
35 Koma Yakobo ndi Yohane, ana aamuna awiri a Zebedayo,+ anapita kwa iye ndi kumuuza kuti: “Mphunzitsi, tikufuna mutichitire chimene tikupempheni.”+