Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye akhale ngati malo opatulika.+ Koma kwa nyumba zonse ziwiri za Isiraeli, iye akhale ngati mwala wopunthwitsa ndiponso ngati mwala wokhumudwitsa.+ Akhalenso ngati msampha ndi khwekhwe kwa anthu okhala mu Yerusalemu.+

  • Maliko 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kodi iyeyu si mmisiri wamatabwa,+ mwana wa Mariya,+ komanso m’bale wake wa Yakobo,+ Yosefe, Yudasi ndi Simoni?+ Ndipo alongo ake si awa omwe tili nawo pompano?” Choncho anayamba kukhumudwa naye.+

  • Luka 7:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Wodala ndi amene sanapunthwe chifukwa cha ine.”+

  • Yohane 6:61
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Koma Yesuyo, pakuti anadziwa payekha kuti ophunzira ake akung’ung’udza pa mawuwo, anafunsa kuti: “Kodi mawuwa mwakhumudwa+ nawo?

  • 1 Akorinto 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 koma ife timalalikira za Khristu amene anapachikidwa.+ Kwa Ayuda, chimenechi ndi chinthu chokhumudwitsa+ ndipo kwa mitundu ina ndi kupusa.+

  • 1 Petulo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 komanso “mwala wopunthwitsa ndi thanthwe lokhumudwitsa.”+ Anthu amenewa akupunthwa chifukwa samvera mawu, ndipo anaikidwiratu kale kuti adzatero.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena