Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 13:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma zofesedwa pamiyala, ndi munthu amene wamva mawu ndi kuwavomereza mwamsanga ndiponso mwachimwemwe.+

  • Mateyu 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Komabe pa iye yekha alibe mizu ndipo amapitirizabe kwa kanthawi. Koma pamene chisautso kapena mazunzo zayamba chifukwa cha mawuwo, iye amapunthwa mwamsanga.+

  • Maliko 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma dzuwa litakwera, mbewuzo zinawauka ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena