Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘Usavule mkazi wa m’bale wako,+ chifukwa kumeneko n’kuvula m’bale wako.

  • Levitiko 20:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mwamuna akakwatira mkazi wa m’bale wake, wachita chinthu chonyansa.+ Iye wavula m’bale wake. Mwamuna ndi mkaziyo ayenera kufa kuti asabereke ana.

  • Mateyu 14:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Anachita zimenezi chifukwa Yohane anali kumuuza kuti: “N’kosaloleka kutenga mkaziyu kuti akhale mkazi wanu.”+

  • Aheberi 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ukwati ukhale wolemekezeka kwa onse, ndipo pogona pa anthu okwatirana pakhale posaipitsidwa,+ pakuti Mulungu adzaweruza adama ndi achigololo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena